Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 5:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Choncho mkazi wake Zeresi ndiponso anzake onsewo anamuuza kuti: “Mukonzetse mtengo wautali mikono 50.* Ndiyeno mawa mʼmawa mukauze mfumu kuti Moredikayi apachikidwe pamtengowo.+ Mukatero mukapite ndi mfumu kuphwandoko kukasangalala.” Hamani anaona kuti maganizo amenewa ndi abwino, choncho anakonzetsa mtengowo.

  • Esitere 7:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Choncho Hamani anamupachika pamtengo umene anakonzera Moredikayi, ndipo mkwiyo wa mfumu unatha.

  • Esitere 9:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Choncho mfumu inalamula kuti achite zimenezo ndipo lamulo linaperekedwa ku Susani.* Komanso ana aamuna 10 a Hamani anapachikidwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena