Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 103:15, 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Masiku a moyo wa munthu ali ngati masiku a udzu.+

      Iye amaphuka ngati duwa lakutchire.+

      16 Koma mphepo ikawomba limafa,

      Ndipo zimangokhala ngati panalibepo.*

  • Yesaya 40:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Tamvera! Winawake akunena kuti: “Lengeza mofuula!”

      Wina akufunsa kuti: “Ndilengeze mofuula za chiyani?”

      “Anthu onse ali ngati udzu wobiriwira.

      Chikondi chawo chonse chokhulupirika chili ngati duwa lakutchire.+

  • Yakobo 1:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 ndipo wachuma asangalale chifukwa waphunzira kukhala wodzichepetsa,+ chifukwa mofanana ndi duwa lakutchire, iye adzafota. 11 Dzuwa likatuluka limatentha kwambiri nʼkufotetsa zomera ndipo maluwa a zomerazo amathothoka moti kukongola kwake kumatha. Mofanana ndi zimenezi munthu wachumayo adzafa ali mkati mofunafuna chuma.+

  • 1 Petulo 1:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Pakuti “anthu onse ali ngati udzu, ndipo ulemerero wawo wonse uli ngati duwa lakutchire. Udzu umafota ndipo duwa limathothoka,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena