Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 73:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndithudi, izi nʼzimene oipa amachita, amakhala mosatekeseka nthawi zonse.+

      Iwo amawonjezera chuma chawo.+

  • Salimo 73:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Iwo awonongedwa mwadzidzidzi.+

      Afika pamapeto awo modzidzimutsa ndipo atha momvetsa chisoni!

  • Mateyu 24:38, 39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Mʼmasiku amenewo Chigumula chisanafike, anthu ankadya ndi kumwa. Amuna ankakwatira ndipo akazi ankakwatiwa mpaka tsiku limene Nowa analowa mʼchingalawa.+ 39 Anthu ananyalanyaza zimene zinkachitika mpaka Chigumula chinafika nʼkuwaseseratu onsewo.+ Zidzakhalanso choncho ndi kukhalapo kwa Mwana wa munthu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena