Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 19:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mukadzalandira cholowa mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani kuti likhale lanu musamadzasunthe zizindikiro za malire a mnzanu,+ pamalo amene makolo anu anaika kale malire.

  • Deuteronomo 27:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 ‘Wotembereredwa ndi munthu wosuntha chizindikiro cha malire a mnzake.’+ (Anthu onse azidzayankha kuti, ‘Zikhale momwemo!’)

  • Miyambo 23:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Usamasunthe chizindikiro chakalekale cha malire,+

      Kapena kulowerera munda wa ana amasiye.

  • Hoseya 5:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Akalonga a Yuda ali ngati anthu osuntha malire.+

      Ndidzawakhuthulira mkwiyo wanga ngati madzi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena