Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 9:22-24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Zonsezi mfundo yake ndi imodzi. Nʼchifukwa chake ndikunena kuti,

      ‘Iye amawononga onse, osalakwa* komanso oipa.’

      23 Anthu atafa mwadzidzidzi ndi madzi osefukira,

      Iye angaseke anthu osalakwa akuvutika.

      24 Dziko lapansi laperekedwa mʼmanja mwa anthu oipa.+

      Iye amaphimba maso a oweruza* a dzikolo.

      Ngati si iyeyo, ndiye ndi ndani?

  • Yobu 34:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Chifukwa wanena kuti, ‘Munthu sapindula chilichonse

      Akamayesetsa kuchita zosangalatsa Mulungu.’+

  • Salimo 73:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndithudi, ndayeretsa mtima wanga pachabe,

      Ndipo ndasamba mʼmanja mwanga pachabe posonyeza kuti ndine wosalakwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena