Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 51:12, 13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 “Ineyo ndi amene ndikukutonthoza.+

      Ndiye nʼchifukwa chiyani ukuopa munthu woti adzafa+

      Ndiponso mwana wa munthu amene adzanyale ngati udzu wobiriwira?

      13 Nʼchifukwa chiyani ukuiwala Yehova amene anakupanga,+

      Amene anatambasula kumwamba+ ndi kuyala maziko a dziko lapansi?

      Ndipo tsiku lonse unkangokhalira kuopa mkwiyo wa amene amakupondereza,

      Ngati kuti ali ndi mphamvu zoti akanatha kukuwononga.

      Kodi tsopano mkwiyo wa amene ankakupondereza uja uli kuti?

  • 1 Petulo 4:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Choncho amene akuvutika chifukwa choti akuchita zimene Mulungu amafuna, apereke moyo wawo kwa Mlengi wathu amene ndi wokhulupirika nʼkumapitiriza kuchita zabwino.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena