Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 42:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Masana Yehova adzandisonyeza chikondi chake chokhulupirika,

      Ndipo usiku ndidzamuimbira nyimbo, ndidzapemphera kwa Mulungu amene amandipatsa moyo.+

  • Salimo 149:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Anthu okhulupirika asangalale chifukwa Mulungu amawalemekeza.

      Iwo aimbe mosangalala ali pamabedi awo.+

  • Machitidwe 16:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Koma chapakati pa usiku, Paulo ndi Sila anayamba kupemphera ndiponso kutamanda Mulungu poimba nyimbo,+ moti akaidi ena ankawamva.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena