Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 33:16-18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Pa nthawi imeneyi mʼpamene amatsegula anthu makutu,+

      Ndipo amadinda* malangizo ake mʼmaganizo mwawo,

      17 Pofuna kubweza munthu kuti asachite zoipa+

      Komanso kumuteteza kuti asakhale wonyada.+

      18 Mulungu amateteza moyo wake kuti usapite kudzenje,*+

      Amateteza munthu kuti asawonongedwe ndi lupanga.*

  • Yesaya 1:19, 20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mukakhala ndi mtima wofuna kundimvera,

      Mudzadya zinthu zabwino za mʼdziko lanu.+

      20 Koma mukakana nʼkupanduka,

      Mudzawonongedwa ndi lupanga,+

      Chifukwa pakamwa pa Yehova mʼpamene panena zimenezi.”

  • Aroma 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Koma anthu amene amakonda mikangano, satsatira choonadi komanso amachita zosalungama, Mulungu adzawasonyeza mkwiyo wake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena