Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 104:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Mikango yamphamvu* imabangula pofunafuna nyama,+

      Ndipo imapempha chakudya kwa Mulungu.+

  • Salimo 145:15, 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Zamoyo zonse zimayangʼana kwa inu mwachiyembekezo.

      Mumazipatsa chakudya pa nyengo yake.+

      פ [Pe]

      16 Mumatambasula dzanja lanu

      Nʼkukwaniritsa zolakalaka za chamoyo chilichonse.+

  • Nahumu 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mkango unkakhadzula nyama yokwanira kuti udyetse ana ake.

      Ndipo unkapha nyama kuti upatse mikango yaikazi.

      Mapanga ake ankakhala odzaza ndi nyama,

      Ndipo mʼmalo ake obisalamo munkakhala nyama zokhadzulakhadzula.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena