Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 23:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Kenako amuna a ku Zifi anapita kwa Sauli ku Gibeya+ nʼkumuuza kuti: “Davide akubisalatu pafupi ndi ife+ kumalo ovuta kufikako ku Horesi,+ paphiri la Hakila+ lomwe lili kumʼmwera* kwa Yesimoni.*+

  • 1 Samueli 26:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Patapita nthawi, amuna a ku Zifi+ anapita kwa Sauli ku Gibeya+ kukamuuza kuti: “Davide akubisala kuphiri la Hakila mbali imene yayangʼanizana ndi Yesimoni.”*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena