Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 19:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Phiri la Sinai linafuka utsi paliponse, chifukwa chakuti Yehova anabwera paphiripo mʼmoto.+ Utsi wakewo unkakwera kumwamba ngati utsi wa uvuni ndipo phiri lonse linkanjenjemera kwambiri.+

  • Oweruza 5:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Yehova, pamene munayenda kuchokera ku Seiri,+

      Pamene munaguba kuchokera kudera la Edomu,

      Dziko linagwedezeka ndipo kumwamba kunagwetsa madzi,

      Mitambo inagwetsa madzi.

       5 Mapiri anasungunuka* pamaso pa Yehova,+

      Ngakhalenso Sinai anasungunuka pamaso pa Yehova,+ Mulungu wa Isiraeli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2026)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena