Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 74:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Kumbukirani anthu* amene munawatenga kalekale kuti akhale anu,+

      Fuko limene munaliwombola kuti likhale cholowa chanu.+

      Kumbukirani phiri la Ziyoni kumene inu mumakhala.+

  • Salimo 132:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Chifukwa Yehova wasankha Ziyoni.+

      Akufunitsitsa kuti akhale malo ake okhalamo. Iye akuti:+

  • Salimo 135:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Yehova amene akukhala ku Yerusalemu,+

      Atamandidwe mu Ziyoni.+

      Tamandani Ya!+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena