Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 10:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma Yehova ndi Mulungu woonadi.

      Iye ndi Mulungu wamoyo+ ndipo ndi Mfumu yamuyaya.+

      Dziko lapansi lidzagwedezeka chifukwa cha mkwiyo wake,+

      Ndipo palibe mitundu ya anthu imene idzapilire mkwiyo wake.

  • Nahumu 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Iye atapsa mtima, ndani angaime pamaso pake?+

      Iye atakwiya, ndani angalimbe mtima kuima pamaso pake?+

      Mkwiyo wake adzaukhuthula ngati moto,

      Ndipo miyala idzaphwanyidwa chifukwa cha iye.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena