Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 63:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Iwo anakumbukira masiku akale,

      Masiku a Mose mtumiki wake,

      Ndipo anafunsa kuti: “Kodi amene anawatulutsa mʼnyanja+ pamodzi ndi abusa a anthu ake+ uja ali kuti?

      Ali kuti amene anaika mzimu wake woyera mwa iye?+

  • Machitidwe 7:35, 36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Mose yemweyo, amene iwo anamukana nʼkunena kuti, ‘Ndani anakupatsa udindo woti uzitilamulira komanso kutiweruza?’+ ndi amene Mulungu anamutumiza+ ngati wolamulira ndi mpulumutsi kudzera mwa mngelo amene anaonekera kwa iye pachitsamba chaminga chija. 36 Munthu ameneyo anawatsogolera nʼkutuluka nawo+ ndipo anachita zodabwitsa ndi zizindikiro ku Iguputo,+ pa Nyanja Yofiira+ ndiponso mʼchipululu kwa zaka 40.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena