Salimo 44:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Munathamangitsa anthu a mitundu ina ndi dzanja lanu,+Ndipo dziko lawo munalipereka kwa makolo athu.+ Munagonjetsa mitundu ya anthu nʼkuithamangitsa.+ Salimo 78:55 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 55 Iye anathamangitsa mitundu ya anthu kuichotsa pamaso pawo.+Iye anawagawira dzikolo kuti likhale cholowa chawo pochita kuwayezera ndi chingwe.+Anachititsa mafuko a Isiraeli kuti akhale mʼnyumba zawozawo.+ Yeremiya 2:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Ine ndinakudzala ngati mtengo wa mpesa wofiira,+ wabwino kwambiri umene unamera kuchokera ku mbewu yabwino kwambiri.Ndiye wandisinthira bwanji nʼkukhala mphukira zachabechabe za mtengo wa mpesa wachilendo?’+
2 Munathamangitsa anthu a mitundu ina ndi dzanja lanu,+Ndipo dziko lawo munalipereka kwa makolo athu.+ Munagonjetsa mitundu ya anthu nʼkuithamangitsa.+
55 Iye anathamangitsa mitundu ya anthu kuichotsa pamaso pawo.+Iye anawagawira dzikolo kuti likhale cholowa chawo pochita kuwayezera ndi chingwe.+Anachititsa mafuko a Isiraeli kuti akhale mʼnyumba zawozawo.+
21 Ine ndinakudzala ngati mtengo wa mpesa wofiira,+ wabwino kwambiri umene unamera kuchokera ku mbewu yabwino kwambiri.Ndiye wandisinthira bwanji nʼkukhala mphukira zachabechabe za mtengo wa mpesa wachilendo?’+