Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 4:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Choncho Yehova anawapereka* kwa Yabini mfumu ya ku Kanani,+ amene ankalamulira ku Hazori. Mkulu wa gulu lake lankhondo anali Sisera, ndipo ankakhala ku Haroseti-ha-goimu.+

  • Oweruza 4:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ine ndidzabweretsa kwa iwe kumtsinje* wa Kisoni,+ Sisera mkulu wa gulu lankhondo la Yabini, pamodzi ndi magaleta ake ankhondo ndi asilikali ake ndipo ndidzamʼpereka mʼmanja mwako.’”+

  • Oweruza 4:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Zitatero Yehova anasokoneza Sisera,+ magaleta ake onse ankhondo komanso asilikali ake onse pamaso pa Baraki. Kenako Sisera anatsika mʼgaleta lake nʼkuyamba kuthawa wapansi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena