Ezara 2:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Awa ndi anthu amʼchigawo* amene anatuluka mu ukapolo+ pa anthu omwe Nebukadinezara mfumu ya ku Babulo anawatengera ku Babulo.+ Anthuwa anabwerera ku Yerusalemu ndi ku Yuda, aliyense kumzinda wakwawo.+ Yeremiya 30:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Yehova wanena kuti: “Ndikusonkhanitsa anthu amʼmatenti a Yakobo amene anagwidwa nʼkutengedwa kupita kudziko lina,+Ndipo ndidzamvera chisoni malo okhala a Yakobo. Mzinda udzamangidwanso pamalo amene unali poyamba,+Ndipo nsanja yokhala ndi mpanda wolimba idzakhala pamalo ake oyenerera. Ezekieli 39:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Choncho Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: ‘Ndidzabwezeretsa ana a Yakobo+ omwe anatengedwa kupita kumayiko ena ndipo ndidzachitira chifundo nyumba yonse ya Isiraeli.+ Ndi mphamvu zanga zonse, ndidzateteza dzina langa loyera.*+
2 Awa ndi anthu amʼchigawo* amene anatuluka mu ukapolo+ pa anthu omwe Nebukadinezara mfumu ya ku Babulo anawatengera ku Babulo.+ Anthuwa anabwerera ku Yerusalemu ndi ku Yuda, aliyense kumzinda wakwawo.+
18 Yehova wanena kuti: “Ndikusonkhanitsa anthu amʼmatenti a Yakobo amene anagwidwa nʼkutengedwa kupita kudziko lina,+Ndipo ndidzamvera chisoni malo okhala a Yakobo. Mzinda udzamangidwanso pamalo amene unali poyamba,+Ndipo nsanja yokhala ndi mpanda wolimba idzakhala pamalo ake oyenerera.
25 Choncho Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: ‘Ndidzabwezeretsa ana a Yakobo+ omwe anatengedwa kupita kumayiko ena ndipo ndidzachitira chifundo nyumba yonse ya Isiraeli.+ Ndi mphamvu zanga zonse, ndidzateteza dzina langa loyera.*+