Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 33:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Iye wandiwombola* kuti ndisapite kudzenje,*+

      Ndipo moyo wanga udzaona kuwala.’

  • Salimo 56:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Chifukwa inu mwandipulumutsa* ku imfa.+

      Ndipo mwateteza phazi langa kuti lisapunthwe,+

      Kuti ndiyende pamaso pa Mulungu mʼkuwala kumene kumaunikira anthu amoyo.+

  • Salimo 116:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Inu mwandipulumutsa ku imfa,

      Mwapukuta misozi yanga ndipo mwateteza phazi langa kuti lisapunthwe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena