Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 19:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Abale anga enieni wawathamangitsira kutali ndi ine,

      Ndipo anthu amene akundidziwa akundisala.+

  • Salimo 31:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Adani anga onse amandinyoza,+

      Makamaka anthu oyandikana nawo.

      Ndipo anthu ondidziwa amachita nane mantha.

      Akandiona ndili panja amandithawa.+

  • Salimo 38:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Anzanga komanso anthu amene ndimawakonda akundisala chifukwa cha mliri wanga,

      Ndipo anthu oyandikana nawo sakufuna kukhala nane pafupi.

  • Salimo 142:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Yangʼanani kudzanja langa lamanja ndipo muone

      Kuti palibe aliyense amene akusamala za ine.*+

      Palibenso kulikonse kumene ndingathawire,+

      Ndipo palibe amene akundidera nkhawa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena