Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 6:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Pamwamba pake panali aserafi. Mserafi aliyense anali ndi mapiko 6. Aliyense anaphimba nkhope yake ndi mapiko awiri, anaphimba mapazi ake ndi mapiko awiri ndipo mapiko ena awiriwo ankaulukira.

       3 Aliyense ankauza mnzake kuti:

      “Woyera, woyera, woyera ndi Yehova wa magulu ankhondo akumwamba.+

      Dziko lonse lapansi ladzaza ndi ulemerero wake.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena