Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 8:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Koma mukadzaiwala Yehova Mulungu wanu nʼkutsatira milungu ina, kuitumikira ndiponso kuigwadira, ndikukuchenjezani lero kuti anthu inu mudzatha ndithu.+

  • Salimo 97:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Onse amene akutumikira chifaniziro chilichonse achite manyazi,+

      Amene amadzitama chifukwa cha milungu yawo yopanda pake.+

      Muweramireni,* inu milungu yonse.+

  • Yona 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Anthu okhulupirira mafano opanda pake, amasiya Mulungu amene angawasonyeze chikondi chokhulupirika.*

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena