Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 95:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 95 Bwerani, tiyeni tifuule kwa Yehova mosangalala!

      Tiyeni tifuule mosangalala ndipo titamande Thanthwe la chipulumutso chathu.+

       2 Tiyeni tikaonekere pamaso pake moyamikira.+

      Tiyeni timuimbire nyimbo zomutamanda ndipo tifuule mosangalala.

  • Salimo 98:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Dziko lonse lapansi lifuulire Yehova mosangalala chifukwa wapambana.

      Kondwerani ndipo fuulani mosangalala komanso imbani nyimbo zomutamanda.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena