Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 65:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Inu mumasamalira dziko lapansi,

      Mumalichititsa kuti libale zipatso zambiri* komanso kuti likhale lachonde.+

      Mtsinje wochokera kwa Mulungu ndi wodzadza ndi madzi.

      Mumachititsa kuti dziko lapansi lipereke chakudya kwa anthu,+

      Umu ndi mmene dziko lapansi munalipangira.

  • Machitidwe 14:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Komabe iye sanangokhala wopanda umboni+ wakuti anachita zabwino. Anakupatsani mvula kuchokera kumwamba ndi nyengo zimene zokolola zanu zimakhala zambiri.+ Anadzaza mitima yanu ndi chakudya komanso chisangalalo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena