Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 1:29, 30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Kenako Mulungu anati: “Ndakupatsani zomera zonse zimene zili padziko lapansi zobereka mbewu komanso mitengo yonse yobereka zipatso zokhala ndi nthangala kuti zikhale chakudya chanu.+ 30 Ndapereka zomera zonse kuti zikhale chakudya+ cha nyama iliyonse yamʼtchire padziko lapansi, chamoyo chilichonse chouluka mumlengalenga komanso chokwawa chilichonse chapadziko lapansi chimene chili ndi moyo.” Ndipo zinaterodi.

  • Genesis 9:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mukhoza kudya chamoyo chilichonse choyenda padziko lapansi.+ Monga mmene ndinakupatsirani zomera zonse kuti zikhale chakudya chanu, ndikukupatsaninso zonsezi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena