Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 16:14-18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Iye ndi Yehova Mulungu wathu.+

      Ziweruzo zake zili padziko lonse lapansi.+

      15 Kumbukirani pangano lake mpaka kalekale,

      Lonjezo limene anapereka ku mibadwo 1,000,+

      16 Kumbukirani pangano limene anapangana ndi Abulahamu,+

      Komanso lumbiro limene analumbira kwa Isaki.+

      17 Pangano limene analikhazikitsa monga lamulo kwa Yakobo,+

      Komanso monga pangano lokhalapo mpaka kalekale kwa Isiraeli,

      18 Pamene anati: ‘Ndidzakupatsa dziko la Kanani,+

      Kuti likhale cholowa chako.’+

  • Yesaya 26:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Usiku ndimakulakalakani ndi mtima wanga wonse,

      Inde, ndimakufunafunani ndi mtima wonse.+

      Chifukwa mukaweruza dziko lapansi,

      Anthu okhala mʼdzikoli amaphunzira zokhudza chilungamo.+

  • Chivumbulutso 15:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Popeza inu nokha Yehova* ndinu wokhulupirika, ndi ndani amene sadzakuopani komanso kulemekeza dzina lanu?+ Anthu a mitundu yonse adzabwera kudzalambira pamaso panu,+ chifukwa iwo adziwa malamulo anu olungama.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena