-
Machitidwe 7:4, 5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
4 Choncho anasamuka mʼdziko la Akasidi nʼkukakhala ku Harana. Kumeneko, bambo ake atamwalira,+ Mulungu anamuuza kuti asamukire mʼdziko lino limene inu mukukhala panopa.+ 5 Koma sanamʼpatsemo cholowa chilichonse, ngakhale kadera kakangʼono. Mʼmalomwake anamulonjeza kuti adzamupatsa dzikoli kuti likhale cholowa chake, ndi cha mbadwa* zake,+ ngakhale kuti pa nthawiyo analibe mwana.
-