Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Hoseya 5:14, 15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ine ndidzakhala ngati mkango wamphamvu kwa Efuraimu,

      Ndiponso ngati mkango wamphamvu kwa anthu a mʼnyumba ya Yuda.

      Ineyo ndidzawakhadzulakhadzula nʼkuchoka.+

      Ndidzawatenga nʼkukawataya ndipo palibe adzawalanditse.+

      15 Kenako ndidzabwerera kumalo anga mpaka iwo atakumana ndi zotsatira za zolakwa zawo,

      Ndipo adzayamba kundifunafuna kuti ndiwakomere mtima.+

      Akadzakumana ndi mavuto, adzandifuna.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena