Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 57:7-11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ndatsimikiza mtima, Inu Mulungu,+

      Ndatsimikiza mtima.

      Ndidzakuimbirani nyimbo ndi zipangizo zoimbira.

       8 Dzuka, iwe ulemerero wanga.

      Dzuka, iwe choimbira cha zingwe, ndi iwenso zeze.

      Ine ndidzadzuka mʼbandakucha.+

       9 Ndidzakutamandani pakati pa mitundu ya anthu, inu Yehova.+

      Ndidzaimba nyimbo zokutamandani pakati pa mitundu ya anthu.+

      10 Chifukwa chikondi chanu chokhulupirika nʼchachikulu moti chafika kumwamba,+

      Ndipo kukhulupirika kwanu kwafika kuthambo.

      11 Inu Mulungu, kwezekani kupitirira kumwamba.

      Ulemerero wanu ukhale padziko lonse lapansi.+

  • Salimo 104:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Ndidzaimbira Yehova+ moyo wanga wonse.

      Ndidzaimba nyimbo zotamanda Mulungu wanga nthawi yonse ya moyo wanga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena