Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 15:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Abisalomu ankadzuka mʼmawa kwambiri nʼkukaima mʼmbali mwa msewu wopita kugeti la mzinda.+ Ndiyeno munthu aliyense akafika ndi mlandu woti uweruzidwe ndi mfumu,+ Abisalomu ankamuitana nʼkumufunsa kuti: “Wachokera mzinda uti?” Munthuyo ankamuuza fuko la Isiraeli limene wachokera. 3 Kenako Abisalomu ankamuuza kuti: “Zimene ukunenazi ndi zoona komanso zomveka. Koma kwa mfumu kulibe aliyense woti amvetsere nkhani yakoyi.”

  • Salimo 31:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Milomo yonena mabodza isowe chonena,+

      Milomo imene imalankhula modzikweza komanso monyoza wolungama.

Mabuku a Chichewa (1974-2026)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena