Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 119:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Zikanakhala bwino ndikanakhala wolimba*+

      Kuti nditsatire malangizo anu.

       6 Zikanatero sindikanachita manyazi,+

      Pa nthawi imene ndikuganizira malamulo anu onse.

  • 1 Yohane 2:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Tsopano inu ana anga okondedwa, khalanibe ogwirizana naye kuti akadzaonekera, tidzakhale ndi ufulu wa kulankhula.+ Komanso kuti tisadzachoke pamaso pake mwamanyazi pa nthawi ya kukhalapo* kwake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena