Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 97:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Inu amene mumakonda Yehova, muzidana ndi zoipa.+

      Iye amateteza moyo wa anthu ake okhulupirika.+

      Amawapulumutsa mʼmanja mwa* oipa.+

  • Salimo 101:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Sindidzayangʼana chinthu chilichonse choipa.*

      Ndimadana ndi zochita za anthu amene asiya kuchita zinthu zabwino.+

      Sindidzalola kuti zochita zawozo zindikhudze.

  • Miyambo 8:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kuopa Yehova kumatanthauza kudana ndi zoipa.+

      Ndimadana ndi kudzikweza, kunyada,+ njira yoipa ndiponso mawu achinyengo.+

  • Miyambo 13:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Wolungama amadana ndi mabodza,+

      Koma zochita za munthu woipa zimabweretsa manyazi ndi kunyozeka.

  • Aroma 12:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Chikondi chanu chisakhale chachiphamaso.+ Muzinyansidwa ndi zoipa+ nʼkumayesetsa kuchita zabwino.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena