-
1 Mbiri 28:9Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
9 Ndipo iwe Solomo mwana wanga, dziwa Mulungu wa bambo wako ndipo uzimutumikira ndi mtima wonse+ komanso mosangalala, chifukwa Yehova amafufuza mitima yonse+ ndipo amazindikira maganizo a munthu ndi zolinga zake zonse.+ Ukamufunafuna, adzalola kuti umupeze,+ koma ukamusiya iye adzakusiya mpaka kalekale.+
-
-
Salimo 95:10Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
10 Kwa zaka 40, mʼbadwo umenewo unkandinyansa ndipo ndinati:
“Awa ndi anthu amene mitima yawo imasochera nthawi zonse,
Njira zanga sakuzidziwa.”
-