Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 19:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Chilamulo cha Yehova ndi changwiro,+ chimabwezeretsa mphamvu.*+

      Zikumbutso za Yehova ndi zodalirika,+ zimapatsa nzeru munthu wosadziwa zinthu.+

  • Miyambo 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Miyambi ya Solomo+ mwana wa Davide,+ mfumu ya Isiraeli:+

  • Miyambo 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Yothandiza munthu wosadziwa zinthu kuti akhale wozindikira.+

      Yothandiza wachinyamata kuti akhale wodziwa zinthu komanso kuti aziganiza bwino.+

  • 2 Timoteyo 3:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kuyambira pamene unali wakhanda,+ wadziwa malemba oyera+ amene angakupatse nzeru zokuthandiza kuti udzapulumuke chifukwa chokhulupirira Khristu Yesu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena