Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 10:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Kenako anamuuza kuti: “Tiye tipitire limodzi ukaone kuti sindilekerera zoti anthu azipikisana* ndi Yehova.”+ Choncho Yehonadabu anapita limodzi ndi anthuwo mʼgaleta lankhondo la Yehu.

  • Salimo 69:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Kudzipereka kwanga panyumba yanu kuli ngati moto umene ukuyaka mumtima mwanga,+

      Ndipo chipongwe cha anthu amene amakunyozani chandigwera.+

  • Yohane 2:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ophunzira ake anakumbukira zimene Malemba amanena kuti: “Kudzipereka kwanga panyumba yanu kudzakhala ngati moto umene ukuyaka mumtima mwanga.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena