Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 30:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Davide anali ndi nkhawa kwambiri chifukwa anthu ankakambirana zoti amuponye miyala. Anthuwo ankafuna kuchita zimenezi chifukwa anakwiya kwambiri ndi kutengedwa kwa ana awo aamuna ndi aakazi. Koma Davide anakhulupirira Yehova Mulungu wake ndipo anapeza mphamvu.+

  • Salimo 62:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 62 Ndithudi, ndikuyembekezera* Mulungu modekha.

      Chipulumutso changa chimachokera kwa iye.+

  • Yesaya 30:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Chifukwa Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, Woyera wa Isiraeli, wanena kuti:

      “Mukabwerera kwa ine nʼkukhala odekha, mudzapulumuka.

      Mudzakhala amphamvu mukakhala odekha komanso mukasonyeza kuti mukundidalira.”+

      Koma inu simunafune.+

  • Maliro 3:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndi bwino kuti munthu akhale chete*+ nʼkumayembekezera chipulumutso cha Yehova.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena