Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 3:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Pa nthawi imeneyo tinalanda dziko la mafumu awiri a Aamori+ amene ankakhala mʼdera la Yorodano, kuyambira mʼchigwa cha Arinoni* mpaka kuphiri la Herimoni.+ 9 (Phiri limeneli Asidoni ankalitchula kuti Sirioni, pamene Aamori ankalitchula kuti Seniri.)

  • 1 Mbiri 5:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Anthu a hafu ya fuko la Manase+ ankakhala kuyambira ku Basana mpaka ku Baala-herimoni, ku Seniri ndi kuphiri la Herimoni+ ndipo anachuluka kwambiri.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena