Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 9:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Amenewa anali oimba, atsogoleri a nyumba za makolo a Alevi mʼzipinda zodyera. Iwo sankapatsidwa ntchito zina chifukwa ankagwira ntchito yawo masana komanso usiku.

  • 1 Mbiri 23:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Chifukwa mogwirizana ndi malangizo omaliza a Davide, Alevi oyambira zaka 20 kupita mʼtsogolo, anawerengedwa.

  • 1 Mbiri 23:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Mʼmawa uliwonse ankaimirira+ kuti athokoze ndi kutamanda Yehova. Madzulo ankachitanso zimenezi.+

  • Luka 2:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Tsopano anali mkazi wamasiye ndipo anali ndi zaka 84 koma sankasowa pakachisi. Ankachita utumiki wopatulika masana ndi usiku ndipo ankasala kudya komanso kupemphera mopembedzera.

  • Chivumbulutso 7:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Nʼchifukwa chake ali pamaso pa mpando wachifumu wa Mulungu. Iwo akumuchitira utumiki wopatulika usana ndi usiku mʼkachisi wake, ndipo Amene wakhala pampando wachifumuyo+ adzawaphimba ndi tenti yake kuti awateteze.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena