Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 1:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Buku la Chilamulo ili lisachoke pakamwa pako.+ Uziliwerenga ndi kuganizira mozama* masana ndi usiku, kuti uzitsatira bwinobwino zonse zimene zalembedwamo.+ Ukamatero, zizikuyendera bwino ndipo uzichita zinthu mwanzeru.+

  • Salimo 119:97
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 97 Ndimakonda kwambiri chilamulo chanu!+

      Ndimaganizira mozama* chilamulocho tsiku lonse.+

  • 1 Timoteyo 4:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Uziganizira mozama* zinthu zimenezi ndipo uzizichita modzipereka kuti anthu onse aone kuti ukupita patsogolo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena