Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Koma si mmene oipa alili.

      Iwo ali ngati mankhusu* amene amauluzika ndi mphepo.

  • Miyambo 10:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Zabwino zimene munthu wolungama ankachita zikakumbukiridwa* amadalitsidwa,+

      Koma dzina la anthu oipa lidzawola.+

  • 2 Petulo 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Zimenezi zikusonyeza kuti Yehova* amadziwa kupulumutsa anthu odzipereka kwa iye akakhala pa mayesero.+ Koma anthu osalungama amawasunga kuti adzawawononge pa tsiku lopereka chiweruzo,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena