Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Akorinto 9:20-22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Kwa Ayuda ndinakhala ngati Myuda, kuti ndithandize Ayuda.+ Kwa anthu otsatira Chilamulo ndinakhala ngati wotsatira Chilamulo kuti ndithandize anthu otsatira chilamulo, ngakhale kuti sinditsatira Chilamulo.+ 21 Kwa anthu amene sayendera Chilamulo ndinakhala ngati wosayendera Chilamulo, kuti ndithandize anthu osayendera Chilamulo. Ndinachita zimenezi ngakhale kuti ndimatsatira malamulo a Mulungu komanso lamulo la Khristu.+ 22 Kwa ofooka ndinakhala wofooka, kuti ndithandize ofooka.+ Ndakhala zinthu zonse kwa anthu osiyanasiyana, kuti ndiyesetse mmene ndingathere kupulumutsa ena.

  • Yakobo 5:19, 20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Abale anga, ngati wina pakati panu wasiya choonadi chifukwa chosocheretsedwa, ndiye munthu wina nʼkumubweza, 20 dziwani kuti amene wabweza wochimwayo panjira yake yoipa,+ wamupulumutsa ku imfa ndipo Mulungu adzakhululukira wochimwayo machimo ambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena