Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 28:15-18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Sizingagulidwe ndi golide woyenga bwino,

      Ndipo munthu sangapereke siliva kuti apeze nzeru.+

      16 Sangazigule ndi golide wa ku Ofiri,+

      Kapena mwala wosowa wa onekisi ndi wa safiro.

      17 Nzeru sitingaziyerekezere ndi golide komanso galasi,

      Ndipo sitingazisinthanitse ndi mbale ya golide woyenga bwino.+

      18 Miyala yamtengo wapatali ya korali ndi kulusitalo sitingaiyerekezere nʼkomwe ndi nzeru.+

      Ndipo thumba lodzaza ndi nzeru ndi lamtengo wapatali kuposa thumba lodzaza ndi ngale.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena