Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 22:17, 18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kenako Sauli anauza asilikali othamanga amene anali atamuzungulira kuti: “Iphani ansembe a Yehova chifukwa ali kumbali ya Davide! Iwo ankadziwa kuti Davide akuthawa, koma sanandiuze!” Komabe atumiki a mfumuwo sanafune kupha ansembe a Yehova. 18 Ndiyeno mfumu inauza Doegi+ kuti: “Iwe, ipha ansembewa!” Nthawi yomweyo Doegi wa ku Edomu+ anapha ansembewo. Tsiku limenelo anapha amuna 85 ovala efodi wa nsalu.+

  • 1 Mafumu 2:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Kenako Mfumu Solomo inauzidwa kuti: “Yowabu wathawira kuchihema cha Yehova ndipo ali pambali pa guwa lansembe.” Choncho Solomo anatuma Benaya mwana wa Yehoyada kuti: “Pita ukamuphe!”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena