Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 14:41, 42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Ndiyeno Sauli anauza Yehova kuti: “Inu Mulungu wa Isiraeli, tiyankheni kudzera mwa Tumimu!”+ Atatero, Yonatani ndi Sauli anasankhidwa ndipo anthuwo anaoneka kuti alibe mlandu. 42 Kenako Sauli anati: “Chitani maere+ pakati pa ine ndi Yonatani mwana wanga.” Zitatero, maerewo anagwera Yonatani.

  • Machitidwe 1:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Kenako anapemphera kuti: “Inu Yehova,* mumadziwa mitima ya anthu onse,+ tisonyezeni amene mwamusankha pa anthu awiriwa

  • Machitidwe 1:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Atatero anachita maere+ ndipo maerewo anagwera Matiya. Choncho iye anamuphatikiza pa atumwi 11 aja.*

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena