Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 32:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Mukamuuzenso kuti, ‘Ndiponso kapolo wanu Yakobo ali mʼmbuyo mwathumu.’” Popeza mumtima mwake anati: “Ngati angasangalale ndi mphatso imene ndatumizayi,+ ndiye kuti ndikakumana naye akhoza kundilandira bwino.”

  • 2 Samueli 16:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Davide atamaliza kukwera phiri lija,+ anapeza Ziba+ mtumiki wa Mefiboseti+ akumudikira kuti akumane naye. Iye anali ndi abulu awiri okhala ndi zishalo atanyamula mikate 200, makeke 100 a mphesa, makeke 100 a zipatso zamʼchilimwe* ndiponso mtsuko waukulu wa vinyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena