Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 23:7, 8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kenako Balamu ananena ndakatulo yakuti:+

      “Balaki mfumu ya Mowabu wandibweretsa kuno kuchokera ku Aramu,+

      Kuchokera kumapiri akumʼmawa kuti:

      ‘Bwera, udzanditembererere Yakobo.

      Bwera, udzaitanire tsoka pa Isiraeli.’+

       8 Ndingathe bwanji kutemberera anthu amene Mulungu sanawatemberere?

      Ndipo ndingathe bwanji kuitanira tsoka anthu amene Yehova sanawaitanire tsoka?+

  • Miyambo 19:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Munthu amakhala ndi mapulani ambiri mumtima mwake,

      Koma zolinga za Yehova nʼzimene zidzakwaniritsidwe.+

  • Machitidwe 5:38, 39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Choncho mmene zinthu zilili apapa, ndikukuuzani kuti asiyeni anthu amenewa musalimbane nawo. Chifukwa ngati zolinga zawo kapena ntchito iyi ikuchokera kwa anthu, sipita patali. 39 Koma ngati ikuchokera kwa Mulungu, simungathe kuwaletsa.+ Ndipo mukaumirira mukhoza kupezeka kuti mukulimbana ndi Mulungu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena