-
Yobu 36:27Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
27 Iye amakoka madontho a madzi.+
Madonthowo amasintha nʼkukhala nkhungu imene imapanga mvula,
-
Yobu 38:37Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
37 Ndi ndani amene ali wanzeru kwambiri moti angawerenge mitambo,
Kapena ndi ndani amene angapendeketse zosungira madzi zakumwamba?+
-
-
-