Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 6:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Hamani atalowa, mfumu inamufunsa kuti: “Kodi tingamuchitire chiyani munthu amene mfumu ikufuna kumupatsa ulemu?” Hamani atamva zimenezi anaganiza kuti: “Kodi winanso ndani amene mfumu ingafune kumupatsa ulemu kuposa ine?”+

  • Esitere 6:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Nthawi yomweyo mfumu inauza Hamani kuti: “Fulumira, tenga chovala ndi hatchi ngati mmene wanenera, ndipo ukachitire zimenezi Moredikayi, Myuda, amene ali kugeti. Uonetsetse kuti wachita zonse zimene wanenazi.”

  • Yakobo 4:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Komabe, kukoma mtima kwakukulu kumene Mulungu amapereka kumaposa khalidwe limeneli. Nʼchifukwa chake lemba limati: “Mulungu amatsutsa odzikuza,+ koma odzichepetsa amawasonyeza kukoma mtima kwake kwakukulu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena