Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 8:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Pa nthawi imeneyo Solomo anasonkhanitsa+ akulu a Isiraeli, atsogoleri a mafuko ndiponso atsogoleri a nyumba za makolo a Aisiraeli.+ Anabwera kwa Mfumu Solomo ku Yerusalemu kuti akatenge likasa la pangano la Yehova ku Mzinda wa Davide,+ komwe ndi ku Ziyoni.+

  • 1 Mafumu 8:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Kenako Solomo anaimirira pafupi ndi guwa lansembe la Yehova kutsogolo kwa Aisiraeli onse ndipo anakweza manja ake mʼmwamba.+

Mabuku a Chichewa (1974-2026)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena