Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 13:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Babulo, amene ndi waulemerero kwambiri* kuposa maufumu onse,+

      Chinthu chokongola chimene Akasidi amachinyadira,+

      Adzakhala ngati Sodomu ndi Gomora pa nthawi imene Mulungu anawononga mizindayi.+

  • Yeremiya 50:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Chifukwa cha mkwiyo wa Yehova, mʼdzikomo simudzakhalanso anthu.+

      Dziko lonselo lidzakhala bwinja.+

      Aliyense wodutsa pafupi ndi Babulo adzayangʼanitsitsa mwamantha

      Ndipo adzamuimbira mluzu chifukwa cha miliri yake yonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena