Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 26:67
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 67 Ndiyeno anayamba kumulavulira kunkhope+ komanso kumumenya nkhonya.+ Ena anamuwomba mbama+

  • Maliko 14:65
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 65 Ndipo ena anayamba kumulavulira,+ kumuphimba nkhope nʼkumamukhoma nkhonya. Iwo ankamuuza kuti: “Losera!” Atamuwomba mbama, asilikali apakhoti anamutenga.+

  • Luka 22:63
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 63 Tsopano amuna amene anagwira Yesu aja anayamba kumuchitira zachipongwe+ komanso kumumenya.+

  • Yohane 18:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Atanena zimenezi, mmodzi wa alonda amene anaima chapafupi anamenya Yesu mbama+ nʼkunena kuti: “Ungamuyankhe choncho wansembe wamkulu?”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena